Listen

Description

9 “Chifukwa chake pempherani motere:

“ ‘Atate athu akumwamba,

dzina lanu lilemekezedwe,

10 Ufumu wanu ubwere,

chifuniro chanu chichitike

pansi pano monga kumwamba.

11 Mutipatse chakudya chathu chalero.

12 Mutikhululukire mangawa athu,

monga ifenso tawakhululukira amangawa athu.

13 Ndipo musatitengere kokatiyesa;

koma mutipulumutse kwa woyipayo.’